nse-x-ngoni_1ti_text_reg/05/17.txt

1 line
265 B
Plaintext

\v 17 \v 18 Lekani azikulu olamulila bwino atolewe oyenela ulemu ukulene, maka-maka bala ogwila nchito yo lalikila mau na ku phunzisa. Pakuti malemba yakuti, "Usaike ng'ombe cingwe kukamwa ngati yupuntha tiligu" nakuti "Ogwila nchito oyenela kupiwa malipilo yake."