nya-x-nyanja_rev_text_reg/22/14.txt

1 line
258 B
Plaintext

\v 14 odala iwo amene asuka zovala zao kuti ankhale na umwai wakudya mu mtengo wa moyo na kungena mu mzinda kungenela pa khomo. \v 15 kunja kuli ma imbwa, ba boza, ba chigololo, bakupaya banzao, bopembeza mafano na bonse bamene bakonda kucita zinthu za boza.