nya-x-nyanja_rev_text_reg/18/18.txt

1 line
436 B
Plaintext

\v 18 banalira pamene banaona chusi cha kupya kwake. banakamba ati, ̈ ni muzinda wabwanji wamene uli ngati muzinda wampamvu?̈ \v 19 bataya dothi pa mitu zao, na kulira mwampamvu, ̈ tsoka, tsoka ku muzinda wa mphamvu wamene bonse benzeli na bwato banalemela na chuma chake. pakuti pa ola imozi chabe aonongeka.̈ \v 20 kondwerani na yeve, kumwamba, inu okulupilira, atumwi na apolofeti, pakuti mulungu abweresa chiweruzo pa yeve!̈