nya-x-nyanja_rev_text_reg/12/11.txt

1 line
344 B
Plaintext

\v 11 Banamugonjesa kupitila mu magazi ya Nkhosa na mau ya umboni wao, chifukwa sibanakonde myoyo zabo kufikila mpaka imfa. \v 12 Chifukwa cha ichi kondwelani, imwe mwamba na bonse bamene mulimo! Koma soka ku ziko yapansi na nyanja, chifukwa mdyelekezi agwela pansi pamene imwe mulili! Eve azula na ukali oipisisa chifukwa ali na ntawi ingóno!