nya-x-nyanja_rev_text_reg/10/01.txt

1 line
376 B
Plaintext

\c 10 \v 1 Pamene apo ninaona m'ngelo wina wamphamvu aseluka kucokela ku mwamba. Anavimbiwa na mukumbi, panali futi na uta wa leza pa mwamba pa mutu wake. Cinso cake cinali ngati zuba na mapazi yake yenze monga vipilala va mulilo. \v 2 Anali naka buku kakang'ono mu manja yake yamene yinali yosegula, na kuika kwendo la ku kwanja la manja pa cimumana na yakumanzele pa mtunda.