nya-x-nyanja_rev_text_reg/05/08.txt

1 line
199 B
Plaintext

\v 8 Pamene mwana wa nkhosa anatenga buku, za moyo zinai ndi akulu 24 anagwa pansi kumulambira. Aliyense anali na mtolilo na mbale yodzala ndi zinthu zonunkhira, yomwe ni ma pemphero ya okhulupilira.