nya-x-nyanja_rev_text_reg/02/01.txt

1 line
381 B
Plaintext

\c 2 \v 1 Kwa mngelo wa mpingo wa ku Efeso lemba: aya ndiye mau ya amene anyamula nyale 7 ku zanja la manja na amene ayenda pakati pa zoikapo nyale 7 za golide, \v 2 "niziba zamene wachita na nchito zanu za mphamvu na kupilira mtima kwanu. Niziba ati simunyengelera banthu oipa. Niziba ati munayesa onse amene amaziyesa a positoli, koma si apositoli, elo mwabapeza kuti ni ba boza.