diff --git a/12/title.txt b/12/title.txt new file mode 100644 index 0000000..dfe3d1f --- /dev/null +++ b/12/title.txt @@ -0,0 +1 @@ +Mutu 12 \ No newline at end of file diff --git a/14/03.txt b/14/03.txt index ec33e71..b4dc95c 100644 --- a/14/03.txt +++ b/14/03.txt @@ -1 +1 @@ -\v 3 \v 4 \v 5 Anaimba nyimbo zasopano pamaso pa Mulungu, zamoyo zinai na akulu. Kunalibe wina opunzira nyimbo imeneyi koma chabe aja 144,000 omwe anaguliwa pa dziko la pansi. Aba nibaja bamene sanazidese na akazi, cifukwa anazisunga ku chiwelewele. Niyaba amene alondola mwana wa nkhosa kulikonse kwamene ayenda. Awa anaguliwa kuchoka pa anthu ngati ana oyamba a Mulungu ni mwana wa nkhosa. Palibe boza yamene inapezeka mkamwa mwao; niopanda chifukwa. \ No newline at end of file +\v 3 Anaimba nyimbo zasopano pamaso pa Mulungu, zamoyo zinai na akulu. Kunalibe wina opunzira nyimbo imeneyi koma chabe aja 144,000 omwe anaguliwa pa dziko la pansi. \v 4 Aba nibaja bamene sanazidese na akazi, cifukwa anazisunga ku chiwelewele. Niyaba amene alondola mwana wa nkhosa kulikonse kwamene ayenda. Awa anaguliwa kuchoka pa anthu ngati ana oyamba a Mulungu ni mwana wa nkhosa. \v 5 Palibe boza yamene inapezeka mkamwa mwao; niopanda chifukwa. \ No newline at end of file diff --git a/14/06.txt b/14/06.txt index 8529a02..29ae63a 100644 --- a/14/06.txt +++ b/14/06.txt @@ -1 +1 @@ -\v 6 \v 7 Ninaona mngelo wina akuuluka mu mwamba, amene anali na uthenga wa moyo ouza anthu onkhala pa ziko la pansi-ku maiko onse, mitundu yonse, chilankhulo na anthu. Anaitana na mau a mphamvu, "yopani Mulungu na kumupasa ulemelero. Chifukwa nthawi ya chiweruzo chake chafika. Mulambileni, wamene anapanga kumwamba, dziko la pansi, nyanja, na nyenje za manzi." \ No newline at end of file +\v 6 Ninaona mngelo wina akuuluka mu mwamba, amene anali na uthenga wa moyo ouza anthu onkhala pa ziko la pansi-ku maiko onse, mitundu yonse, chilankhulo na anthu. \v 7 Anaitana na mau a mphamvu, "yopani Mulungu na kumupasa ulemelero. Chifukwa nthawi ya chiweruzo chake chafika. Mulambileni, wamene anapanga kumwamba, dziko la pansi, nyanja, na nyenje za manzi." \ No newline at end of file diff --git a/14/09.txt b/14/09.txt index 5ff9ecf..4d57607 100644 --- a/14/09.txt +++ b/14/09.txt @@ -1 +1 @@ -\v 9 \v 10 Mngelo wina-mngelo wachitatu- anawalondola kukamba ati na mau okuwa, "ngati wina apembeza chilombo na chifano chake, na kupasiwa namba pa mphumi kapena pa zanja lake, azamwa vinyo wa mkwiyo wa Mulungu, vinyo wamene waikiwa opanda kutirako manzi mu cup ya kukalipa kwake. Munthu amene azamwa azabvutika na muliro na sufule pamenso pa angelo na mwana wa nkhosa." \ No newline at end of file +\v 9 Mngelo wina-mngelo wachitatu- anawalondola kukamba ati na mau okuwa, "ngati wina apembeza chilombo na chifano chake, na kupasiwa namba pa mphumi kapena pa zanja lake, \v 10 azamwa vinyo wa mkwiyo wa Mulungu, vinyo wamene waikiwa opanda kutirako manzi mu cup ya kukalipa kwake. Munthu amene azamwa azabvutika na muliro na sufule pamenso pa angelo na mwana wa nkhosa." \ No newline at end of file diff --git a/14/11.txt b/14/11.txt index 025c8f0..f3c5dc8 100644 --- a/14/11.txt +++ b/14/11.txt @@ -1 +1 @@ -\v 11 \v 12 Utsi wa kunzunzika kwao upitilira ku mwamba nthawi zonse, ndipo sapumula usana na usiku-awa opembeza chilombo na fano lake, na aliyese amene analandira chizindikiro cha zina lake. Apa pali kufunika kupilira kwa iwo amene ni oyera, amene akonkha malamulo ya Mulungu na chikhulupiliro mwa Yesu." \ No newline at end of file +\v 11 Utsi wa kunzunzika kwao upitilira ku mwamba nthawi zonse, ndipo sapumula usana na usiku-awa opembeza chilombo na fano lake, na aliyese amene analandira chizindikiro cha zina lake. \v 12 Apa pali kufunika kupilira kwa iwo amene ni oyera, amene akonkha malamulo ya Mulungu na chikhulupiliro mwa Yesu." \ No newline at end of file diff --git a/14/14.txt b/14/14.txt index 3bdaf24..619720c 100644 --- a/14/14.txt +++ b/14/14.txt @@ -1 +1 @@ -\v 14 \v 15 \v 16 Ninayangana, ndipo panali makumbi yoyera. Ndipo onkhala pa makumbi anali ngati mwana wa munthu. Anali na kolona ya golide pa mutu pake na chikwakwa chonola ku manja yake. Ndipo mngelo wina anatuluka mu nyumba ya Mulungu ndipo anaitana na mau okweza kuitana uja amene ali pa makumbi: "Tenga chikwakwa chako elo uyambe kujuba. Chifukwa nthawi yojuba yakwana, cifukwa zokolola pa ziko zapya." Ndipo wamene anali pa makumbi anayamba kuyendesa chikwakwa pa ziko, ndipo ziko inakololedwa. \ No newline at end of file +\v 14 Ninayangana, ndipo panali makumbi yoyera. Ndipo onkhala pa makumbi anali ngati mwana wa munthu. Anali na kolona ya golide pa mutu pake na chikwakwa chonola ku manja yake. \v 15 Ndipo mngelo wina anatuluka mu nyumba ya Mulungu ndipo anaitana na mau okweza kuitana uja amene ali pa makumbi: "Tenga chikwakwa chako elo uyambe kujuba. Chifukwa nthawi yojuba yakwana, cifukwa zokolola pa ziko zapya." \v 16 Ndipo wamene anali pa makumbi anayamba kuyendesa chikwakwa pa ziko, ndipo ziko inakololedwa. \ No newline at end of file diff --git a/14/17.txt b/14/17.txt index 62e4d9f..17323d2 100644 --- a/14/17.txt +++ b/14/17.txt @@ -1 +1 @@ -\v 17 \v 18 Mngelo wina anatuluka ku mwamba mu nyumba ya Mulungu; nayeve anali na chikwakwa. Mngelo winanso anatuluka kuchoka pa guwa la zonunkhirisa, amene anali na ulamuliro pa muliro. Anaitana na mphamvu uja amene anali na chikwakwa chonola, "Tenga chikwakwa chako na kuika pamozi zidunswa za mpesa m'minda ya ziko, chifukwa mpesa wake wapya." \ No newline at end of file +\v 17 Mngelo wina anatuluka ku mwamba mu nyumba ya Mulungu; nayeve anali na chikwakwa. \v 18 Mngelo winanso anatuluka kuchoka pa guwa la zonunkhirisa, amene anali na ulamuliro pa muliro. Anaitana na mphamvu uja amene anali na chikwakwa chonola, "Tenga chikwakwa chako na kuika pamozi zidunswa za mpesa m'minda ya ziko, chifukwa mpesa wake wapya." \ No newline at end of file diff --git a/14/19.txt b/14/19.txt index d23b6d6..7a62f43 100644 --- a/14/19.txt +++ b/14/19.txt @@ -1 +1 @@ -\v 19 \v 20 Mngelo anayendesa chikwakwa chake pa ziko nakutenga zidunswa za mpesa. Anaiponya motwera mpesa wa mkwiyo wa Mulungu. Ndipo motwera mpesa munaponyewa panja pa mzinda, ndipo magazi anathiridwa kuchoka mwaicho kufika pakamwa pa akavalo, ma stadia 1,600. \ No newline at end of file +\v 19 Mngelo anayendesa chikwakwa chake pa ziko nakutenga zidunswa za mpesa. Anaiponya motwera mpesa wa mkwiyo wa Mulungu. \v 20 Ndipo motwera mpesa munaponyewa panja pa mzinda, ndipo magazi anathiridwa kuchoka mwaicho kufika pakamwa pa akavalo, ma stadia 1,600. \ No newline at end of file diff --git a/15/03.txt b/15/03.txt index c92c04e..7def4ab 100644 --- a/15/03.txt +++ b/15/03.txt @@ -1 +1 @@ -\v 3 \v 4 Anali kuimba nyimbo ya Mose, kapolo wa Mulungu, nyimbo ya mwana wa nkhosa: "Nchito zanu ni zabwino komanso za mphamvu, ambuye Mulungu, wa mphamvu zonse. Njira zanu ni zabwino ni za chilungamo, mfumu ya maiko onse. Ndani wamene sazakuyopani, Ambuye, nakukweza zina lanu? Chifukwa inu nokha ndinu oyera. Maiko onse yazabwera kukupembezani cifukwa cha nchito zanu zoyera zomwe zavumbulusidwa." \ No newline at end of file +\v 3 Anali kuimba nyimbo ya Mose, kapolo wa Mulungu, nyimbo ya mwana wa nkhosa: "Nchito zanu ni zabwino komanso za mphamvu, ambuye Mulungu, wa mphamvu zonse. Njira zanu ni zabwino ni za chilungamo, mfumu ya maiko onse. \v 4 Ndani wamene sazakuyopani, Ambuye, nakukweza zina lanu? Chifukwa inu nokha ndinu oyera. Maiko onse yazabwera kukupembezani cifukwa cha nchito zanu zoyera zomwe zavumbulusidwa." \ No newline at end of file diff --git a/manifest.json b/manifest.json index 6297b32..c1f5fc4 100644 --- a/manifest.json +++ b/manifest.json @@ -140,6 +140,21 @@ "11-16", "11-18", "11-19", + "12-title", + "14-title", + "14-03", + "14-06", + "14-08", + "14-09", + "14-11", + "14-13", + "14-14", + "14-17", + "14-19", + "15-title", + "15-01", + "15-02", + "15-03", "17-title" ] } \ No newline at end of file