diff --git a/19/17.txt b/19/17.txt index 7948050..554f465 100644 --- a/19/17.txt +++ b/19/17.txt @@ -1 +1 @@ -\v 17 \v 18 ninaona mungelo oimilira pa zuba. anaitana na mau yamphamvu ku nyoni zonse zouluka mumwamba, "bwerani, munkhale pamozi ku pwando la mulungu. bwerani mudye matupi ya mamfumu, matupi ya akulu a nkhondo, matupi ya banthu ba mphamvu, matupi ya mahosi na bamene bakwerapo, na matupi ya banthu bonse, akapolo na omasuka, banthu bopanda nchito na ba mphamvu." \ No newline at end of file +\v 17 ninaona mungelo oimilira pa zuba. anaitana na mau yamphamvu ku nyoni zonse zouluka mumwamba, "bwerani, munkhale pamozi ku pwando la mulungu. \v 18 bwerani mudye matupi ya mamfumu, matupi ya akulu a nkhondo, matupi ya banthu ba mphamvu, matupi ya mahosi na bamene bakwerapo, na matupi ya banthu bonse, akapolo na omasuka, banthu bopanda nchito na ba mphamvu." \ No newline at end of file diff --git a/19/19.txt b/19/19.txt index 0c26723..e5770d4 100644 --- a/19/19.txt +++ b/19/19.txt @@ -1 +1 @@ -\v 19 \v 20 ninaona chilombo na mamfumu ba pa ziko lapansi na banthu babo ba nkhondo. banakumana kuti bamenye nkhondo na baja bali pa mahosi na bankhondo bake. chilombo chinagwiliwa pamozi na mneneri waboza wamene anachita zodabwisa pamenso pake. na zizindikiro zamene izi ananamiza bonse bamene banalandira cizindikiro cha chilombo na bamene banapembeza chifano chake. bonse babili banaponyedwa mu nyanja ya muliro wa sufule. \ No newline at end of file +\v 19 ninaona chilombo na mamfumu ba pa ziko lapansi na banthu babo ba nkhondo. banakumana kuti bamenye nkhondo na baja bali pa mahosi na bankhondo bake. \v 20 chilombo chinagwiliwa pamozi na mneneri waboza wamene anachita zodabwisa pamenso pake. na zizindikiro zamene izi ananamiza bonse bamene banalandira cizindikiro cha chilombo na bamene banapembeza chifano chake. bonse babili banaponyedwa mu nyanja ya muliro wa sufule. \ No newline at end of file diff --git a/20/07.txt b/20/07.txt index d615b93..28b9e78 100644 --- a/20/07.txt +++ b/20/07.txt @@ -1 +1 @@ -\v 7 \v 8 pamene zaka 1000 zisila, satana azamumasula ku ndende yake. azayenda kunamiza maiko mbali zonse za ziko lapansi-gog na magog kubaleta pamozi kuti bamenye nkhondo. bazankhala bambiri kwati ni dothi la mu manzi. \ No newline at end of file +\v 7 pamene zaka 1000 zisila, satana azamumasula ku ndende yake. \v 8 azayenda kunamiza maiko mbali zonse za ziko lapansi-gog na magog kubaleta pamozi kuti bamenye nkhondo. bazankhala bambiri kwati ni dothi la mu manzi. \ No newline at end of file diff --git a/20/11.txt b/20/11.txt index b3b82e1..a403732 100644 --- a/20/11.txt +++ b/20/11.txt @@ -1 +1 @@ -\v 11 \v 12 ninaona mupando waukulu oyera na wamene anankhalapo. ziko lapansi na kumwamba kunathaba ulemelero wake, koma kunalibe malo yakuti zibisameko. ninaona omwalira-ba mphamvu na opanda nchito-kuimilira pa mpando wa mfumu, mabuku yanaseguliwa. buku inangu inaseguliwa-buku la moyo. banthu bakufa banaweruziwa kulingana na zamene zinalembewa mu mabuku, kulingana na zinchito zawo. \ No newline at end of file +\v 11 ninaona mupando waukulu oyera na wamene anankhalapo. ziko lapansi na kumwamba kunathaba ulemelero wake, koma kunalibe malo yakuti zibisameko. \v 12 ninaona omwalira-ba mphamvu na opanda nchito-kuimilira pa mpando wa mfumu, mabuku yanaseguliwa. buku inangu inaseguliwa-buku la moyo. banthu bakufa banaweruziwa kulingana na zamene zinalembewa mu mabuku, kulingana na zinchito zawo. \ No newline at end of file diff --git a/20/13.txt b/20/13.txt index 517964e..f9c4770 100644 --- a/20/13.txt +++ b/20/13.txt @@ -1 +1 @@ -\v 13 \v 14 \v 15 nyanja zinachosa bamene banaferamo. imfa na hadesi zinachosa bakufa bamene banalimo, elo bakufa banaweruziwa kulingana na zamene banachita. imfa na hadesi zinaponyewa mu nyanja ya muliro. uku nikufa kwa chiwiri- nyanja ya muliro. ngati zina ya wina aliyense sinalembewe mu buku la moyo, anaponyewa mu nyanja ya muliro. \ No newline at end of file +\v 13 nyanja zinachosa bamene banaferamo. imfa na hadesi zinachosa bakufa bamene banalimo, elo bakufa banaweruziwa kulingana na zamene banachita. \v 14 imfa na hadesi zinaponyewa mu nyanja ya muliro. uku nikufa kwa chiwiri- nyanja ya muliro. \v 15 ngati zina ya wina aliyense sinalembewe mu buku la moyo, anaponyewa mu nyanja ya muliro. \ No newline at end of file diff --git a/21/01.txt b/21/01.txt index 30871df..93045f6 100644 --- a/21/01.txt +++ b/21/01.txt @@ -1 +1 @@ -\c 21 \v 1 \v 2 elo ninaona kumwamba kwasopano na ziko lapansi lasopano, cifukwa kumwamba na ziko ya kudala vinapita, na nyanja sizinaliko. ninaona muzinda oyera, yerusalemu wa sopano, zamene zinachoka kumwamba kwa mulungu, kukonzewa monga mkazi wamene akumana na mwamuna wake. \ No newline at end of file +\c 21 \v 1 elo ninaona kumwamba kwasopano na ziko lapansi lasopano, cifukwa kumwamba na ziko ya kudala vinapita, na nyanja sizinaliko. \v 2 ninaona muzinda oyera, yerusalemu wa sopano, zamene zinachoka kumwamba kwa mulungu, kukonzewa monga mkazi wamene akumana na mwamuna wake. \ No newline at end of file diff --git a/21/03.txt b/21/03.txt index d922f91..098a1ef 100644 --- a/21/03.txt +++ b/21/03.txt @@ -1 +1 @@ -\v 3 \v 4 ninamvera mau yochokera ku mpando kukamba kuti, "onani! malo yamene mulungu ankhalako yali na banthu, elo azankhala nabeve. bazankhala banthu bake, elo mulungu mwini wake azankhala nabeve elo azankhala mulungu wao. azapukuta misozi yawo yonse mumenso mwawo, elo sikuzankhala kufa, kulira, kapena kudandaula, kapena kuwawa. zinthu zakudala zapita. \ No newline at end of file +\v 3 ninamvera mau yochokera ku mpando kukamba kuti, "onani! malo yamene mulungu ankhalako yali na banthu, elo azankhala nabeve. bazankhala banthu bake, elo mulungu mwini wake azankhala nabeve elo azankhala mulungu wao. \v 4 azapukuta misozi yawo yonse mumenso mwawo, elo sikuzankhala kufa, kulira, kapena kudandaula, kapena kuwawa. zinthu zakudala zapita. \ No newline at end of file diff --git a/21/05.txt b/21/05.txt index 923ef71..1f6419e 100644 --- a/21/05.txt +++ b/21/05.txt @@ -1 +1 @@ -\v 5 \v 6 wamene anankhala pa mpando anakamba ati, "ona! nipanga zinthu zonse zasopano." anati, "lemba izi pansi chifukwa mau aya ni ya zoona." anakamba naine ati, "izi zinthu zasila! ndine alefa na omega, oyamba na osiliza. kwa wamene amvera njota nizamupasa manzi yosagula kuchoka ku musinje wa manzi ya moyo. \ No newline at end of file +\v 5 wamene anankhala pa mpando anakamba ati, "ona! nipanga zinthu zonse zasopano." anati, "lemba izi pansi chifukwa mau aya ni ya zoona." \v 6 anakamba naine ati, "izi zinthu zasila! ndine alefa na omega, oyamba na osiliza. kwa wamene amvera njota nizamupasa manzi yosagula kuchoka ku musinje wa manzi ya moyo. \ No newline at end of file diff --git a/21/07.txt b/21/07.txt index 6ba3535..ddbf0f4 100644 --- a/21/07.txt +++ b/21/07.txt @@ -1 +1 @@ -\v 7 \v 8 wamene apambana azatenga zinthu zimenezi, elo ine nizankhala mulungu wake, yeve azankhala mwana wanga. koma bamene bachita mantha, opanda chikulupiliro, na okanika, wopaya anzao, bachigololo, ba boza, opembeza mafano malo yawo ni ku nyanja ya muliro wa sufule. iyi ni imfa ya chiwiri." \ No newline at end of file +\v 7 wamene apambana azatenga zinthu zimenezi, elo ine nizankhala mulungu wake, yeve azankhala mwana wanga. \v 8 koma bamene bachita mantha, opanda chikulupiliro, na okanika, wopaya anzao, bachigololo, ba boza, opembeza mafano malo yawo ni ku nyanja ya muliro wa sufule. iyi ni imfa ya chiwiri." \ No newline at end of file diff --git a/21/09.txt b/21/09.txt index df6c5a3..fb8a6b3 100644 --- a/21/09.txt +++ b/21/09.txt @@ -1 +1 @@ -\v 9 \v 10 m'mozi wa angelo bali 7 anabwera kwa ine, wamene anali na mbale 7 zozula na zilango zosiliza, anakamba kwa ine, "bwera kuno. nizakulangiza mkazi, mkazi wa mwana wa nkhosa." ananitenga mu mzimu kuyenda ku lupili itali nakunilangiza muzinda oyera yerusalemu kuseluka kuchoka ku mwamba kwa mulungu. \ No newline at end of file +\v 9 m'mozi wa angelo bali 7 anabwera kwa ine, wamene anali na mbale 7 zozula na zilango zosiliza, anakamba kwa ine, "bwera kuno. nizakulangiza mkazi, mkazi wa mwana wa nkhosa." \v 10 ananitenga mu mzimu kuyenda ku lupili itali nakunilangiza muzinda oyera yerusalemu kuseluka kuchoka ku mwamba kwa mulungu. \ No newline at end of file diff --git a/21/11.txt b/21/11.txt index 0698caa..b9a0d85 100644 --- a/21/11.txt +++ b/21/11.txt @@ -1 +1 @@ -\v 11 \v 12 \v 13 yerusalemu anali na ulemelero wa mulungu, na kuwala kwake kunali monga mphete, monga mwala wa bafuta wa jesipa. unali na mpanda waukulu, na polowera 12, na angelo pa khomo. pa makomo onse panalembewa maina ya mitundu 12 ya ana a israele. ku m'mawa kunali makomo atatu, kumpoto kunali makomo atatu, ku m'mwera kunali makomo atatu komanspo kumazulo kunali makomo atatu. \ No newline at end of file +\v 11 yerusalemu anali na ulemelero wa mulungu, na kuwala kwake kunali monga mphete, monga mwala wa bafuta wa jesipa. \v 12 unali na mpanda waukulu, na polowera 12, na angelo pa khomo. pa makomo onse panalembewa maina ya mitundu 12 ya ana a israele. \v 13 ku m'mawa kunali makomo atatu, kumpoto kunali makomo atatu, ku m'mwera kunali makomo atatu komanspo kumazulo kunali makomo atatu. \ No newline at end of file diff --git a/21/14.txt b/21/14.txt index 5b412ba..81b1f50 100644 --- a/21/14.txt +++ b/21/14.txt @@ -1 +1 @@ -\v 14 \v 15 mpanda wa mzinda unali ni maziko 12, pa izo panali maina 12 ya apositoli a mwana wa nkhosa. wamene anakamba na ine anali na kopimila kopangiwa na golide kamene anapimila mzinda, makomo na mpanda wake. \ No newline at end of file +\v 14 mpanda wa mzinda unali ni maziko 12, pa izo panali maina 12 ya apositoli a mwana wa nkhosa. \v 15 wamene anakamba na ine anali na kopimila kopangiwa na golide kamene anapimila mzinda, makomo na mpanda wake. \ No newline at end of file diff --git a/manifest.json b/manifest.json index 69adad6..8b66d67 100644 --- a/manifest.json +++ b/manifest.json @@ -195,6 +195,25 @@ "19-07", "19-09", "19-11", - "19-14" + "19-14", + "19-17", + "19-19", + "19-21", + "20-title", + "20-01", + "20-04", + "20-05", + "20-07", + "20-09", + "20-11", + "20-13", + "21-title", + "21-01", + "21-03", + "21-05", + "21-07", + "21-09", + "21-11", + "21-14" ] } \ No newline at end of file