nya-x-nyanja_rev_text_reg/05/03.txt

1 line
384 B
Plaintext
Raw Normal View History

\v 3 \v 4 \v 5 Palibe aliyense kumwamba, padziko la pansi kapena pansi pa dziko yemwe anali oyenera kusegula buku kapena kuwerenga. Ninalira maningi chifukwa panalibe aliyense oyenera kusegula kapena kuwerenga buku. Koma m'mozi wa akulu-akulu anati kwa ine, "Usalire. Ona! nkhalamu ya mtundu wa ayuda, muzu wa Davide, wapambana. Akwanisa kusegula buku na kusegula zosindikizira zake."