nya-x-nyanja_rev_text_reg/19/07.txt

1 line
273 B
Plaintext
Raw Normal View History

\v 7 \v 8 tiyeni tikondwere na kunkhala okondwa na kumupasa ulemu chifukwa chisangalalo cha ukwati wa mwana wa nkhosa chafika, elo mkazi wa chikwati wakonzeka. analoledwa kuti abvale zovala zowala na zopanda dothi" (chifukwa zovala zopanda dothi ni zincito za anthu oyera).