\v 6 6Ni ciani cilikubwera kucokera kucipululu ngati chusi, ozola ngati mure, na lubani, na unga wathunthu wogulitsidwa na amalonda? \v 7 Onani, ni pa bedi ya Solomo; Ankhondo makumi asanu nai modzi azunguluka, Amuna amphamvu a mu Israeli.