1 line
345 B
Plaintext
1 line
345 B
Plaintext
\v 8 Pali mafumukazi makumi asanu na imodzi, na bakazi bafana bosabelengeka. \v 9 Nkhunda yanga, ilibe choipa, ndiye yeka; ndiye mwana mukazi umodzi yeka waba mai bake; ndiye mwana eka mukazi wamene anabala; Basikana anamuwona ndipo anamuitana odalisika; mfumukazi na azimai adamuwonanso, ndipo adamtamanda: Zomwe mfumukazi ndi adzakazi adanena |