nya-x-nyanja_sng_text_reg/05/08.txt

1 line
180 B
Plaintext

\v 8 Ndikulumbirirani, ana akazi inu a ku Yerusalemu, kuti, mukapeza bwenzi langa, mudzamdziwitsa chiyani? - Ndidwala chifukwa cha chikondi. Akazi amzindawu akuyankhula ndi mkaziyo