|
\v 6 Mkazi akudziyankhulila yekha 6Ndi ciani cikukwera kucokera kucipululu ngati utsi, wakudzola ndi mure, ndi lubani, ndi ufa wathunthu wogulitsidwa ndi amalonda? \v 7 Taonani, ndi kama wa Solomo; Ankhondo makumi asanu ndi limodzi akuzungulira, Amuna amphamvu a mu Israeli. |