1 line
288 B
Plaintext
1 line
288 B
Plaintext
\v 12 Maluwa yaonekela paziko lapansi; ntawi yodulia na kuimba kwa nyoni yafika, ndipo phokoso ya nkhunda yamveka mudziko yatu. \v 13 Mutengo wa mkuyu yapya nkhuyu wake yobiriwira, ndipo mipesa yachita maluwa; zipereka fungo yake. Nyamuka, okodewa wanga, wokongola wanga, tiye tiziyenda. |