nya-x-nyanja_sng_text_reg/02/08.txt

1 line
251 B
Plaintext

\v 8 Pali phokoso pali okondewa wanga! Mvelani, apa abwela, akudumpha pamapiri, nakujumpha pamapiri. \v 9 Wokondewa wanga ali ngati mbawala kapena mwana wa mphoyo; onani, wayimirira kuseli kwa khoma lathu, akuyang'anisisa pazenera, asuzumila pazenela.