1 line
295 B
Plaintext
1 line
295 B
Plaintext
\v 12 Maluwawo awonekera padziko lapansi; nthawi yodulira ndi kuimba kwa mbalame yafika, ndipo phokoso la nkhunda lamveka m'dziko lathu. \v 13 Mtengo wa mkuyu upsa nkhuyu zake zobiriwira, ndipo mipesa yachita maluwa; amapereka fungo lawo. Nyamuka, bwenzi langa, wokongola wangawe, tiye tizipita. |