nya-x-nyanja_sng_text_reg/02/05.txt

1 line
241 B
Plaintext

\v 5 Nditsitsimutseni ndi makeke a mphesa ndipo munditsitsimutse ndi maapurikoti, chifukwa ndatopa ndi chikondi. Mkazi ameneyu amalankhula yekha \v 6 Dzanja lake lamanzere lili kunutu kwa mutu wanga, ndipo dzanja lake lamanja landikumbatira.