\v 5 Nditsitsimutseni ndi makeke a mphesa ndipo munditsitsimutse ndi maapurikoti, chifukwa ndatopa ndi chikondi. Mkazi ameneyu amalankhula yekha \v 6 Dzanja lake lamanzere lili kunutu kwa mutu wanga, ndipo dzanja lake lamanja landikumbatira.