1 line
290 B
Plaintext
1 line
290 B
Plaintext
\v 12 Maluwa yaonekera paziko lapansi; nthawi yodulira na kuimba kwa nyoni yafika, ndipo phokoso ya nkhunda ylamveka m'dziko yathu. \v 13 Mtengo wa mkuyu yapya nkhuyu wake yobiriwira, ndipo mipesa yachita maluwa; zipereka fungo lawo. Nyamuka, bwenzi langa, wokongola wangawe, tiye tizipita. |