nya-x-nyanja_sng_text_reg/05/03.txt

1 line
209 B
Plaintext

\v 3 "Navula mkanjo wanga; ndiyeneranso kuuvekanso? Ndasambitsa mapazi anga; kodi ndiwadetse?" \v 4 Wokondedwa wanga analowetsa dzanja lake pakhomo la chitseko, ndipo mtima wanga unakhudzidwa chifukwa cha iye.