nya-x-nyanja_sng_text_reg/06/13.txt

1 line
196 B
Plaintext

\v 13 Bwerera, bwerera m'mbuyo, Msulami iwe! Bwerera, tibwerere kuti tikakuyang'ane! Mkazi amene akuyankhula ndi anzakewo N'chifukwa chiyani mwaona Msulami, ngati kuti mukuvina gombe la Mahanaimu?