nya-x-nyanja_sng_text_reg/04/15.txt

1 line
285 B
Plaintext

\v 15 Iwe ndiwe kasupe wamaluwa, kasupe wamadzi abwino, mitsinje ikuyenda kuchokera ku Lebanoni. \v 16 bwera, mphepo yakumwera; ipani m'munda mwanga kuti zonunkhira zake zizitulutsa kununkhira kwake. Mulole wokondedwa wanga alowe m'munda wake kuti adzadye zipatso zake zokoma kwambiri.