1 line
308 B
Plaintext
1 line
308 B
Plaintext
\v 5 Ndine ofipa koma wokondewa, ana akazi imwe a ku Yerusalemu; ofipa ngati mahema ya Kedara, okongola ngati nsalu za Solomoni. \v 6 Musaniyang'ane chifukwa ndine ofipa, chifukwa zuba shoka ine. mwana mwuna wanga anakalipa naine; Banani ika oyang'anila minda yamphesa, koma sininasunge munda wanga wamphesa. |