nya-x-nyanja_sng_text_reg/06/11.txt

1 line
262 B
Plaintext

\v 11 Nina kumunda wamitengo kuti nika one kakulidwe kamene kali mumalo, kuti nika one ngati mipesa inaphukila, kapena ngati makangaza yali pachimake. \v 12 Ninali wokondwa kwambiri kuti ndimamva kuti ndinkakwera galeta la kalonga abwenzi akuyankhula ndi mayiyo