nya-x-nyanja_sng_text_reg/03/06.txt

1 line
239 B
Plaintext

\v 6 6Ni ciani cilikubwera kucokera kucipululu ngati chusi, ozola ngati mure, na lubani, na unga wathunthu wogulitsidwa na amalonda? \v 7 Onani, ni pa bedi ya Solomo; Ankhondo makumi asanu nai modzi azunguluka, Amuna amphamvu a mu Israeli.