nya-x-nyanja_sng_text_reg/08/11.txt

1 line
319 B
Plaintext

\v 11 Solomo anali ndi munda wamphesa ku Baal Hamon. Anapereka mundawo kwa iwo amene adzausamalira. Aliyense anayenera kubweretsa ndalama zasiliva zokwana 1,000. \v 12 Munda wanga wamphesa, wanga womwe, uli pamaso panga; masekeli chikwi chimodzi ndi anu, Solomo, ndipo masekeli mazana awiriwo ndi a osunga zipatso zake.