nya-x-nyanja_sng_text_reg/01/05.txt

1 line
312 B
Plaintext

\v 5 Ndine ofipa koma wokondewa, ana akazi imwe a ku Yerusalemu; ofipa ngati mahema a Kedara, okongola ngati nsalu za Solomo. \v 6 Musaniyang'ane chifukwa ndili ndi mdima, chifukwa zuwa laniwotcha ine. Bana aamuna banga anakwiya nane; Ananiyika woyang'anira minda yamphesa, koma sininasunge munda wanga wamphesa.