nya-x-nyanja_sng_text_reg/07/12.txt

1 line
198 B
Plaintext

\v 12 Tiye tiuke kuseniseni tiyende ku minda ya mphesa; tiye tikaone ngati mipesa yaphuka, kaya maluba yake yaseguka, kapena ngati makangaza yali na maluba. Kwamenekuja niza kupasa chikondi changa.