nya-x-nyanja_sng_text_reg/08/11.txt

1 line
340 B
Plaintext

\v 11 Solomoni anali na munda wampesa ku Baal Hamoni. Anapasa munda wampesa kuli bamene banga isamalile. Aliyense anali kuyenela kubwelesa mashekeli yasiliva yokwana 1,000 yazi paso zake \v 12 Munda wanga wamphesa, wanga wamene, uli pamenso panga; mashekeli 1,000 ni yako, Solomoni, ndipo mashekeli yali 100 niya abo bosunga zipaso zake.