nya-x-nyanja_sng_text_reg/06/11.txt

1 line
235 B
Plaintext

\v 11 Nina yenda ku munda wamitengo kuti nika one ka kulidwe ka mene kali mumalo, kuti nika one ngati mipesa ina pukila, kapena ngati makangaza yali pachimake. \v 12 Sinina zibe pamene moyo wanga unani ika pa galeta yabantu bolemeka.