nya-x-nyanja_sng_text_reg/06/02.txt

1 line
211 B
Plaintext

\v 2 Okondewa wanga ayenda kumunda wake, po gona zonunkila, kuti udye munda naku ika pamozi maluba. \v 3 Ndine wa okondewa wanga, ndipo okondewa wanga ni wanga; Akudya musipu pakati pa maluba na chisangalalo.