\v 8 Pali phokoso pali okondewa wanga! Mvelani, apa abwela, akudumpha pamapili, nakujumpha pamapili. \v 9 Okondewa wanga ali kwati mbawala kapena mwana wa mphoyo; onani, wayimilila kuseli kwa khoma yathu, akuyang'anisisa pazenela, asuzumila pazenela.