1 line
236 B
Plaintext
1 line
236 B
Plaintext
|
\v 16 Wokondedwa wanga ndi wanga, ndipo ine ndine wake; Mkaziyo akuyankhula ndi mwamunayo \v 17 Pita, wokondedwa wanga, mphepo yam'bandakucha isanagwe ndi mithunzi isanachoke. Chokani; khala ngati mphoyo, kapena nswala pa mapiri olimba.
|