nya-x-nyanja_rev_text_reg/11/10.txt

1 line
498 B
Plaintext

\v 10 Bamene bankala pa ziko ya pansi baza kondwela pali yeve naku sangalala. Baza pasana na mpaso chifukwa aba baneneri babili bana vutisa bantu benzo nkala pa ziko. \v 11 Koma pakapita ma siku yatatu na siku yosa kwanila mpepo ya moyo yochoka kuli Mulungu izabangena, ndipo baza imilala pa mendo yabo. Kuyopa kukulu kuzagwera bonse baza baona. \v 12 Ndipo bazamvela liu ikulu kuchoka ku mwamba kubauza, "Bwera pamwamba pano!" Ndipo baza yenda kumwamba mu makumbi, pamene badani babo ba yanganila.