nya-x-nyanja_rev_text_reg/17/08.txt

1 line
369 B
Plaintext

\v 8 chinyama chamene unaona chenzeko, apa manje kulibe, koma chili pafupi kubweranso kuchoka ku chimugodi chamene chilibe polekezera. elo chizayenda kuononga. onse bamene bankhala pa ziko, bonse bamene mazina yao mulibe mu buku la moyo kucoka poyamba pa ziko-bazankhala odabwa pamene bazaona chilombo chimenechi chifukwa chenzeko, apa manje kulibe, koma chizabweranso.