nya-x-nyanja_rev_text_reg/13/09.txt

1 line
269 B
Plaintext

\v 9 Ngati aliyense ali na kwatu, mulekeni amvele. \v 10 Ngati aliyense aenela kutengewa ukapolo, ku ukapolo aza enda. Ngati ali yense ayenela kupaiwa na mupeni, na mupeni azapaiwa. Uku nikuitaniwa kuti mupilire molimbikila ma chikulupiliro kwa bantu boyela ba Mulungu.