nya-x-nyanja_rev_text_reg/05/11.txt

1 line
275 B
Plaintext

\v 11 Ndipo ninaona ndi kumva mau ya angelo ambiri kuzungulira mpando wa chimfumu, zamoyo zinai ndi akulu 24. Unyinji wao unali zikwi ndi zikwi. \v 12 Ananena mu mau okweza, "Ndi oyenera mwana wa nkhosa yemwe anaphedwa kulandira mphamvu, ulemelero,nzeru, ulemu na matamando."