nya-x-nyanja_rev_text_reg/08/13.txt

1 line
221 B
Plaintext

\v 13 Ninaona, ndipo ninamva mphungu yomwe imauluka pakati pa mitambo, kuitana na mau yokweza, "tsoka, tsoka, tsoka, kwa amene ankhala pa dziko la pansi, chifukwa cha malipenga omwe asalira kuti alizidwe na angelo atatu."