nya-x-nyanja_rev_text_reg/10/08.txt

1 line
349 B
Plaintext

\v 8 Mau ninamvera kucokela ku mwamba yanalankhulanso kuli ine: "Pita, tenga buku losegula imene ili mu kwanja ya mngelo woimilila pa mumana na pa ziko." \v 9 Pamene apo ninayenda ku mungelo nakumuuza kuti anipase ka buku kakang'ono. Anakamba na ine, "Tenga buku na kudya. Izapanga mmala mwako ku baba, koma mkamwa mwako izankala yonzuna ngati uci."