nya-x-nyanja_rev_text_reg/22/08.txt

1 line
347 B
Plaintext

\v 8 ine, yohane, ndine wamene ninamvera na kuona zinthu izi. pamene ninamvera na kuona, ninagwa pansi ku mapazi ya mungelo kuti nimupembeze, na mungelo wamene ananilangiza izi zinthu. \v 9 anakamba kwa ine, "usacite tero! naine ndine kapolo kwati iwe, na abale bako baneneri. na bonse bamene bamvera mau yamene yali mu buku iyi, pembeza mulungu!"