nya-x-nyanja_rev_text_reg/10/03.txt

1 line
282 B
Plaintext

\v 3 Pamene apo anapunda namau yopundisa monga ku uluma kwa mkango. Pamene anapunda, zo gunda 7 vinakamba nakuuluma kwake. \v 4 Pamene vogunda 7 vinakamba, nenze pafupi na kulemba, koma ninamvela mau kucokela ku mwamba yakunena, "Sunga nkama ya vimene vogunda 7 vanena. Usavilembe."