nya-x-nyanja_rev_text_reg/22/01.txt

1 line
337 B
Plaintext

\c 22 \v 1 mungelo ananilangiza musinje wa manzi ya moyo, yoyera maningi. manzi yanali kuyenda kuchoka ku mpando wa mulungu na mwana wa nkhosa \v 2 kupita pakati pa mseu wa mzinda. mbali iliyose ya msinje kunali mutengo wa moyo, obala zipaso 12 za mitundu yosiyana, ndipo ubala zipaso mwezi ulionse. mayani ya mtengo ni yocirisila maiko.