nya-x-nyanja_rev_text_reg/15/03.txt

1 line
400 B
Plaintext

\v 3 Anali kuimba nyimbo ya Mose, kapolo wa Mulungu, nyimbo ya mwana wa nkhosa: "Nchito zanu ni zabwino komanso za mphamvu, ambuye Mulungu, wa mphamvu zonse. Njira zanu ni zabwino ni za chilungamo, mfumu ya maiko onse. \v 4 Ndani wamene sazakuyopani, Ambuye, nakukweza zina lanu? Chifukwa inu nokha ndinu oyera. Maiko onse yazabwera kukupembezani cifukwa cha nchito zanu zoyera zomwe zavumbulusidwa."