nya-x-nyanja_rev_text_reg/13/15.txt

1 line
519 B
Plaintext

\v 15 Anavomelezewa kupasa moyo ku chifanikizo cha chilombo mwakuti chifanikizo chija chikazikwanisa kukamba na kulenga bonse bamene banakana kupembeza chilombo kuti bapaiwe. \v 16 China kakamiza bantu bonse, bamene sibochuka nabaja bochuka, bolemela nabaja bosauka, bomasuka na bakapolo, kulandila chidindo pa zanja yamanja yaku manja kapena pa mpumi. \v 17 Chinali chovuta kuti muntu aliyense agulise kapena kugula chintu koma ngati anali nacho chidindo cha chilombo, kukamba kuti, numero yamene iimililako zina yake.