nya-x-nyanja_rev_text_reg/12/10.txt

1 line
239 B
Plaintext

\v 10 Ninamvela liu ikulu kumwamba: "Manje chafika chipulumuso na mpavu na ufumu wa Mulungu, na ulamulilo wa Kristu wake. Chifukwa eve onamizila babale batu aponyewa pansi, wamene anali kubanamizila pamenso pa Mulungu watu muzuba na usiku.