nya-x-nyanja_rev_text_reg/07/09.txt

1 line
416 B
Plaintext

\v 9 Pambuyo pa zinthu izi ninaona, ndipo panali anthu ambiri amene palibe angawerenge-kuchoka ku maiko onse, mtundu, anthu na chilankhulo-kuimilira pa mpando wa chimfumu ni mwana wa nkhosa. Anali atamvala zobvala zoyera, ndipo ananyamula nthambi za kanjeza m'manja mwao, \v 10 ndipo anali kukamba na mau okweza: " Chipulumuso chichokera kwa Mulungu wathu amene ankhala pa mpando wa chimfumu ni kwa mwana wa nkhosa!"