nya-x-nyanja_rev_text_reg/05/13.txt

1 line
351 B
Plaintext

\v 13 Ninamva cholengedwa chilichonse kumwamba, padziko la pansi, na pansi pa dziko la pansi ni mu manzi- zonse zopezekamo- kukamba ati, "kwa iye okhala pa mpando wa chimfumu na kwa mwana wa nkhosa, kukhale matamando, ulemu, ulemelero ndi mphamvu zolamulira nthawi zonse." \v 14 Zamoyo zinai zinati, "Amen!" ndipo akulu anazigwesa pansi ndi kulambira.