nya-x-nyanja_rev_text_reg/03/09.txt

1 line
444 B
Plaintext

\v 9 Onani! onse amene achokera ku mpingo wa satana, iwo amene akamba ati ni bayuda koma sibayuda; anama chabe boza. Nizabapanga kuti babwere bagwade pa mapazi yanu, ndipo bazaziba kuti nikukondani. \v 10 Chifukwa mwasunga malamulo anga mopilira, naine nizakusungani pa nthawi ya mayeso yamene ibwera padziko lapansi, kuyesa onse amene ankhala pa dziko. \v 11 Nibwera manje-manje. Sungani bwino zamene muli nazo kuti anthu asalande kolona yanu.