nya-x-nyanja_rev_text_reg/02/20.txt

1 line
320 B
Plaintext

\v 20 Koma nili na kanthu aka pa inu: Mumamulekelera mkazi Yezebeli, amene amazikamba ati ni muneneri. chifukwa cha zopunzisa zake asokoneza bambiri bakapolo banga kuti bazichita chiwelewele, nakudya chakudya chamene chapasidwa kwa vibanda. \v 21 Nimamupasa nthawi kuti aleke zoipa, koma safuna kuleka chiwelewele chake.